Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 6:4 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake, ngati muli nayo milandu ya zinthu za moyo uno, kodi muweruzitsa iwo amene ayesedwa achabe mu Mpingo?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake, ngati muli nayo milandu ya zinthu za moyo uno, kodi muweruzitsa iwo amene ayesedwa achabe mu Mpingo?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ngati muli ndi milandu pa zinthu zotere, bwanji mumaika anthu amene mpingo suŵayesa kanthu kuti aiweruze?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼchifukwa chake, ngati pali milandu pa zinthu zotere, sankhani anthu ena kuti akhale oweruza ngakhale alibe udindo mu mpingo.

Onani mutuwo



1 Akorinto 6:4
4 Mawu Ofanana  

Pakuti nditani nao akunja kukaweruza iwo? Kodi amene ali m'katimo simuwaweruze ndi inu,


Kodi simudziwa kuti tidzaweruza angelo? Koposa kotani nanga zinthu za moyo uno?


Ndinena ichi kukuchititsani inu manyazi. Kodi nkutero kuti mwa inu palibe mmodzi wanzeru, amene adzakhoza kuweruza pa abale,