Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 4:16 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikukupemphani tsono kuti muzinditsanzira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine.

Onani mutuwo



1 Akorinto 4:16
8 Mawu Ofanana  

Khalani onditsanza ine, monga inenso nditsanza Khristu.


Abale, khalani pamodzi akutsanza anga, ndipo yang'anirani iwo akuyenda kotero monga muli ndi ife chitsanzo chanu.


Zimenenso mudaziphunzira, ndi kuzilandira, ndi kuzimva, ndi kuziona mwa ine, zomwezo chitani; ndipo Mulungu wa mtendere adzakhala pamodzi ndi inu.


Ndipo munayamba kukhala akutsanza athu, ndi a Ambuye, m'mene mudalandira mauwo m'chisautso chambiri, ndi chimwemwe cha Mzimu Woyera;


si chifukwa tilibe ulamuliro, komatu kuti tidzipereke tokha tikhale kwa inu chitsanzo chanu, kuti mukatitsanze ife.


Kumbukirani atsogoleri anu, amene analankhula nanu Mau a Mulungu; ndipo poyang'anira chitsiriziro cha mayendedwe ao mutsanze chikhulupiriro chao.


osati monga ochita ufumu pa iwo a udindo wanu, koma okhala zitsanzo za gululo.