Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 16:5 - Buku Lopatulika

Koma ndidzadza kwa inu, nditapyola Masedoniya; pakuti ndidzapyola Masedoniya;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ndidzadza kwa inu, nditapyola Masedoniya; pakuti ndidzapyola Masedoniya;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidzafika kwanuko nditadutsa dziko la Masedoniya, pakuti ndingodzerako ku Masedoniyako.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndidzafika kwanuko nditadutsa ku Makedoniya pakuti ndikuyembekezera kudzera ku Makedoniyako.

Onani mutuwo



1 Akorinto 16:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo zitatha izi, Paulo anatsimikiza mu mzimu wake, atapita pa Masedoniya ndi Akaya, kunka ku Yerusalemu, kuti, Nditamuka komweko ndiyenera kuonanso ku Roma.


Pakuti kunakondweretsa a ku Masedoniya ndi Akaya kuchereza osauka a kwa oyera mtima a ku Yerusalemu.


Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane.


Koma ndidzafika kwa inu msanga, akandilola Ambuye; ndipo ndidzazindikira si mau a iwo odzitukumula, koma mphamvuyi.