Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 15:7 - Buku Lopatulika

pomwepo anaonekera kwa Yakobo; pamenepo kwa atumwi onse;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pomwepo anaonekera kwa Yakobo; pamenepo kwa atumwi onse;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo adaonekera Yakobe, kenaka atumwi onse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anaonekeranso kwa Yakobo, kenaka kwa atumwi onse.

Onani mutuwo



1 Akorinto 15:7
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ananyamuka nthawi yomweyo nabwera ku Yerusalemu, napeza khumi ndi mmodziwo, ndi iwo anali nao atasonkhana pamodzi,


Ndipo pakulankhula izi iwowa, Iye anaimirira pakati pao; nanena nao, Mtendere ukhale nanu.


Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa.


Koma m'mene adawatambasulira dzanja akhale chete, anawafotokozera umo adamtulutsira Ambuye m'ndende. Ndipo anati, Muwauze Yakobo ndi abale izi. Ndipo anatuluka napita kwina.