Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 13:10 - Buku Lopatulika

Koma pamene changwiro chafika, tsono chamderamdera chidzakhala chabe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma pamene changwiro chafika, tsono chamderamdera chidzakhala chabe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

koma changwiro chikadzaoneka, chopereŵeracho chidzatha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma changwiro chikadzaoneka ndipo chopereweracho chidzatha.

Onani mutuwo



1 Akorinto 13:10
9 Mawu Ofanana  

Pompo mwezi udzanyazitsidwa, ndi dzuwa lidzakhala ndi manyazi, pakuti Yehova wa makamu adzalamulira chaulemerero m'phiri la Ziyoni, ndi mu Yerusalemu, ndi pamaso pa akuluakulu ake.


Pamene ndinali mwana, ndinalankhula ngati mwana, ndinalingirira ngati mwana, ndinawerenga ngati mwana; tsopano ndakhala munthu, ndayesa chabe zachibwana.


Pakuti tsopano tipenya m'kalirole, ngati chimbuuzi; koma pomwepo maso ndi maso. Tsopano ndizindikira mderamdera; koma pomwepo ndidzazindikiratu, monganso ndazindikiridwa.


Pakuti ife tidziwa mderamdera, ndimo tinenera mderamdera.


Si kunena kuti ndinalandira kale, kapena kuti ndatha kukonzeka wamphumphu; koma ndilondetsa, ngatinso ndikachigwire ichi chimene anandigwirira Khristu Yesu.