Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 11:9 - Buku Lopatulika

pakutinso mwamuna sanalengedwe chifukwa cha mkazi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pakutinso mwamuna sanalengedwa chifukwa cha mkazi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiponso mwamuna sadalengedwe chifukwa cha mkazi, koma mkazi ndiye adalengedwa chifukwa cha mwamuna.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mwamuna sanalengedwe chifukwa cha mkazi, koma mkazi analengedwera mwamuna.

Onani mutuwo



1 Akorinto 11:9
5 Mawu Ofanana  

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.


Adamu ndipo anazitcha maina zinyama zonse, ndi mbalame za m'mlengalenga ndi zamoyo zonse za m'thengo: koma kwa Adamu sanapezeke womthangatira iye.


Ndipo nthitiyo anaichotsa Yehova Mulungu mwa Adamu anaipanga mkazi, ndipo ananka naye kwa Adamu.


koma mkazi chifukwa cha mwamuna; chifukwa cha ichi mkazi ayenera kukhala nao ulamuliro pamutu pake, chifukwa cha angelo.