Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 11:13 - Buku Lopatulika

Lingirirani mwa inu nokha: Kodi nkuyenera kuti apemphere kwa Mulungu, wosafunda mutu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Lingirirani mwa inu nokha: Kodi nkuyenera kuti apemphere kwa Mulungu, wosafunda mutu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Weruzani nokha ngati nkoyenera kuti mkazi azipembedza Mulungu osavala kanthu kumutu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dziweruzeni. Kodi nʼchabwino kuti mkazi apemphere kwa Mulungu wopanda chophimba kumutu?

Onani mutuwo



1 Akorinto 11:13
5 Mawu Ofanana  

Ndipo inunso, pa nokha mulekeranji kuweruza kolungama?


Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.


Ndinena monga kwa anzeru; lingirirani inu chimene ndinena.


Kodi ubadwidwe womwe sutiphunzitsa kuti ngati mwamuna aweta tsitsi chinyozetsa iye?


Akazi akhale chete mu Mipingo. Pakuti sikuloledwa kwa iwo kulankhula. Koma akhale omvera, monganso chilamulo chinena.