Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 11:1 - Buku Lopatulika

Khalani onditsanza ine, monga inenso nditsanza Khristu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Khalani onditsanza ine, monga inenso nditsanza Khristu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Muzinditsanzira ine monga momwe inenso ndimatsanzira Khristu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsatirani chitsanzo changa, monga inenso nditsatira chitsanzo cha Khristu.

Onani mutuwo



1 Akorinto 11:1
9 Mawu Ofanana  

monga inenso ndikondweretsa onse m'zinthu zonse, wosafuna chipindulo changa, koma cha unyunjiwo, kuti apulumutsidwe.


Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.


Abale, khalani pamodzi akutsanza anga, ndipo yang'anirani iwo akuyenda kotero monga muli ndi ife chitsanzo chanu.


Ndipo munayamba kukhala akutsanza athu, ndi a Ambuye, m'mene mudalandira mauwo m'chisautso chambiri, ndi chimwemwe cha Mzimu Woyera;


si chifukwa tilibe ulamuliro, komatu kuti tidzipereke tokha tikhale kwa inu chitsanzo chanu, kuti mukatitsanze ife.


kuti musakhale aulesi, koma akuwatsanza iwo amene alikulowa malonjezano mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima.