Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 10:2 - Buku Lopatulika

nabatizidwa onse kwa Mose, mumtambo, ndi m'nyanja,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nabatizidwa onse kwa Mose, mumtambo, ndi m'nyanja,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero mumtambomo ndi m'nyanjamo onsewo adachita ngati kubatizidwa ndi kukhala amodzi ndi Mose.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo onse anabatizidwa mwa Mose mu mtambo ndi mʼnyanja.

Onani mutuwo



1 Akorinto 10:2
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Israele anaiona ntchito yaikulu imene Yehova anachitira Aejipito, ndipo anthuwo anaopa Yehova; nakhulupirira Yehova ndi mtumiki wake Mose.


nabatizidwa ndi iye mu mtsinjewo wa Yordani, alikuwulula machimo ao.


Kapena kodi simudziwa kuti ife tonse amene tinabatizidwa mwa Khristu Yesu; tinabatizidwa mu imfa yake?


Pakuti nonse amene munabatizidwa kwa Khristu mudavala Khristu.