Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 10:12 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake iye wakuyesa kuti ali chilili, ayang'anire kuti angagwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake iye wakuyesa kuti ali chilili, ayang'anire kuti angagwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono amene akuganiza kuti waimirira molimba, achenjere kuti angagwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho, ngati mukuganiza kuti mwayima mwamphamvu, samalani mungagwe!

Onani mutuwo



1 Akorinto 10:12
11 Mawu Ofanana  

Kunyada kutsogolera kuonongeka; mtima wodzikuza ndi kutsogolera kuphunthwa.


Wodala munthu wakuopa kosalekeza; koma woumitsa mtima wake adzagwa m'zoipa.


Chifukwa chake yang'anirani mamvedwe anu; pakuti kudzapatsidwa kwa iye amene ali nacho; ndipo kwa iye amene alibe chidzachotsedwa, chingakhale chija aoneka ngati ali nacho.


Chabwino; iwo anathyoledwa ndi kusakhulupirira kwao, ndipo iwe umaima ndi chikhulupiriro chako. Usamadzikuza mumtima, koma opatu:


Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa.


Penyani kuti pasakhale wina wakulanda inu ngati chuma, mwa kukonda nzeru kwake, ndi chinyengo chopanda pake, potsata mwambo wa anthu, potsata zoyamba za dziko lapansi, osati potsata Khristu;


Inu, tsono, okondedwa, pozizindikiratu izi, chenjerani, kuti potengedwa ndi kulakwa kwa iwo osaweruzika, mungagwe kusiya chikhazikiko chanu.