Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 1:22 - Buku Lopatulika

Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo popeza Ayuda afunsa zizindikiro, ndi Agriki atsata nzeru:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ayuda amafuna kuwona zozizwitsa, pamene Agriki amafunafuna nzeru.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ayuda amafuna zizindikiro zodabwitsa ndipo Agriki amafunafuna nzeru,

Onani mutuwo



1 Akorinto 1:22
10 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anapatsa chizindikiro tsiku lomwelo, nati, Chizindikiro chimene Yehova ananena ndi ichi, Taonani guwali la nsembe lidzang'ambika, ndi phulusa lili pa ilo lidzatayika.


Ndipo Afarisi anatuluka, nayamba kufunsana naye, ndi kufuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba, namuyesa Iye.


Koma ena anamuyesa, nafuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba.


Koma ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi chala cha Mulungu, pamenepo Ufumu wa Mulungu wafikira inu.


Chifukwa chake Ayuda anayankha nati kwa Iye, Mutionetsera ife chizindikiro chanji, pakuti muchita izi?


Pamenepo mkazi anasiya mtsuko wake, namuka mumzinda, nanena ndi anthu,


Pamenepo Yesu anati kwa iye, Ngati simuona zizindikiro ndi zozizwa, simudzakhulupirira.