Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa

Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano


Nahumu INTRO1 - Buku Lopatulika Buku Lopatulika
Nahumu INTRO1

1

Mau Oyamba
Bukuli ndi ndakatulo yokondwerera kupasuka kwa Ninive, mzinda waukulu wa Aasiriya amene ankazunza Aisraele kuyambira kale. Kupasuka kwa mzindawo kuwoneka ngati chilango cha Mulungu chogwera anthu onyada ndi ankhanza.
Za mkatimu
Chauta aimba Ninive mlandu 1.1-15
Kupasuka kwa mzindawo 2.1—3.19

Bible Society of Malawi

Bible Society of Malawi