1 Mulungu an'dziwika mu Judha, dzina lake nilikulu mu Izraeli.
Panin'chemela ndidayileni Mulungu wakulungama kwangu, mudanditsudzula pandikhadabzanthiwa. Ndikomeleni ntima mubvembo pemphelo langu.
Wam'phamvu, Mulungu Chawuta, anilewa achichemela dziko lapantsi, kuyambila kumabveladzuwa mpaka kumadokelo.
Mulungu ndichizeni nadzina lanu, namphamvu zanu woneseni kuti ndilibe milandu!
Imwe Mulungu ibvani kulila kwangu, tetekelani pemphelo langu.
Lekani Mulungu atikomele ntima pomwe atidalise! Awinike nkhope yake kwayise! Selah.