1 Imbilani Mulungu nafala lakukondwa dziko lentse!
Chitani chiwowo chakusekelela kwa Chawuta, dziko lentse!
Lekani bzentse bzinfema bzidumbize Chawuta! Aleluya!
Kwawuyo ankwila padzulu pakudzulu kuyambila kale, pomwe antuma fala lake, fala lake lamphamvu.
Imbani, chemelelani kwa Mulungu, m'phamvu zathu! Kuwani, kondwani kwa Mulungu wa Jakobho!
Imbilani Chawuta nyimbo inyowani! Imbilani Chawuta, dziko lentse lapantsi!
Chitani chiwowo chakusekelela Chawuta, dziko lentse! Tsamulani nyimbo yakusekelela, imbani nyimbo zakudumbiza!