3 Mulungu, mumbuto zake zakuchinjilizika, adabziwonesa kuti ndiye an'chinjiliza.
Awo an'themba na Chawuta, aninga phili la Ziyoni, linsaya kutekenyeka, linkhala kufika lini nalini.
Ngaadalisiwe Chawuta kuchoka mu Ziyoni, uyo an'khala mu Jerusalema. Aleluya!
Chawuta Wankhondo ana yise, Mulungu wa Jakobho nipakubisala pathu. Selah.
Mulungu aniyetima kuchoka paphili la Ziyoni, phili labwino kwene-kwene.