4 Niwakudala munthu an'chita Chawuta, chikhulupililo chake. Uyo ansaya kupatukila kwawakubzikuza, kwaawo antayikila kumagunkha.
Imwe muntsimula wakubzikuza, wakutembelelewa, ampatuka pamitemo yanu;
Koma awo ampatukila kunjila zawo zakupotoka, Chawuta an'zaachosa pabodzi nawanthu wakuyipa! Nkhalo ngayiwe pa Izraeli.
An'nyoza awo wakulambiwa na Chawuta, koma anilemekeza an'gopa Chawuta. An'chita bzaaninga alumbila kuti an'zachita, ne panango bzingakhale bzakuwuma tani.
mphsodani mwana. Pakuti angakalipe, muchifela munjila, pomwe an'diza lini kukalipa. Niwakudala awo ampotela kwayiye.
Imbani kwayiye nyimbo inyowani! Lizani mwaluso gitale muchikuwa!
Layidzani muwone kuti Chawuta niwabwino! Niwakudala munthu an'thawila kwayiye.
Ndidatsendamila kwayimwe kuyambila pakubadwa pangu, ndimwe mudandigwata n'chombo, dumbizo langu lin'khala kwayimwe nthawe zentse.