2 Pakuti misewe yanu yanyula mwayine, janja lanu labwela payine.
Pakuti mun'zaathamangisa, mudalata nkhope zawo nawutati wanu.
Pakuti Chawuta usiku namasikati, janja lanu lidandilemela, mphamvu zangu zidamala, ninga kumaliwa nakuphsa kwadzuwa. Selah.
Ndikomeleni ntima, Chawuta pakuti ndatepa, mundilape Chawuta, pakuti mabondo yangu yamala basa.
Koma Mulungu an'zaalasa namisewe yake, mwadzidzimu, achizapwetekeka.