3 Mbani angakwile paphili la Chawuta? Mbani angayime pambuto yake yakuyela?
Chawuta, mbani an'zakhala mutenti yanu? Mbani an'zakhala paphili lanu lakuyela?
“Ndidayikha mambo wangu paphili la Ziyoni, paphili lakuyela.”
Niwakudala bzawo wanthu wam'munsakhula, muchiwabwelesa pafupi, kuti akhale muntalo chanu, tin'zakhuta nakukoma kwanyumba yanu, kwa Tembele yanu yakuyela.
Pamudakwila kumbuto itali, muchitsogolela wakupambiwa, mudatambila mpfupo kuchoka kuwanthu. Ne pakati pawanthu wakupanduka, kuti Chawuta Mulungu akhalemo.