Biblia Todo Logo
အွန်လိုင်း သမ္မာကျမ်းစာ

- ကြော်ငြာတွေ -




Nyimbo 23:3 - Bhukhu la Kuyamba

3 An'zabwezela pakale ntima wangu, an'zanditsogolela mumisewu yakulungama, thangwe ladzina lake.

အခန်းကိုကြည့်ပါ။ ကော်ပီ




Nyimbo 23:3
28 ပူးပေါင်းရင်းမြစ်များ  

Adaachiza nathangwe ladzina lake, kuti awonese ukulu wake.


Koma imwe, Chawuta Mfumu wangu; ndichitileni nathangwe ladzina lanu; pakuti ntsisi zanu n'zabwino, ndipulumuseni!


Ndatsakalila ninga bila latayika, psagani mulanda wanu, pakuti niniyebwa lini mitemo yanu.


Ntemo wa Chawuta niwakukonkholoka, um'bweza umoyo. Ufakazi wa Chawuta ngwakukhulupilika, uchipasa nzelu alibe nzelu.


Pakuti ndimwe pakuthawila pangu, mwala napakubisala pangu, nathangwe ladzina lanu, ndiwoneseni pomwe nditsogoleleni.


Mun'zandichosa muwukonde waadanditeya, pakuti imwe ndimwe mbuto yangu yakupotela.


Ngatikuzeni Chawuta pabodzi nayine, bwelani tisumuse dzina lake pabodzi!


Nditsogoleleni Chawuta muchilungamo chanu, nathangwe laazondi wangu, lungamisani njila yanu patsogolo pangu.


Lengani ntima wakuchena mwayine, imwe Mulungu! Bwezelani n'zimu wakuchinga mwayine!


Ndibwezeleni kusekelela kwachipulumuso chanu! Ndichengeteni nan'zimu wakutetekela!


Tithandizeni, imwe Mulungu wachipulumuso chathu! Kuchitila mbili yadzina lanu; tichizeni, mugwanile bzakuyipa bzathu!


Chilungamo chin'zayenda patsogolo pake, chichizakonzela njila makhalo yake.


ကြှနျုပျတို့နောကျလိုကျပါ:

ကြော်ငြာတွေ


ကြော်ငြာတွေ