3 Lekani adumbize dzina lake nakubvina! Achimuyimbila, achiliza chikhwechele nachipendani!
Mudasandula kulila kwangu kuchikhala kubvina, mudatsudzula bzakubvala bzangu bzamasakha, muchindibvadzika kukondwa.
Tendani Chawuta nachipendani! Mupembezeni nagitale lina mawaya khumi!
Tsamulani nyimbo, lizani chikhwechele! Lizani chipendani nabhanjo!
Lizani wunda pakukhala kwamwezi, pakukhuma kwamwezi, pantsiku yathu yafeshita.
Anyakuyimba naanyakubvina wentse an'zati, “Ntsantsa zathu zili mwayiwe.”