3 Nkazi wako an'zachita ninga muvayini um'bala michelo munyumba mwako, wana wako an'zachita ninga bziphuphu bzamuolivi, kuzungunuka thebulu yako.
“Jozefi ali nin'thayi um'bala, n'thayi um'bala m'mbali mwakamadzi; mithayi yake intambalala padzulu pampanda.
Wonani! Wana ninthaka in'choka kwa Chawuta, n'chelo wamimba nimpagalo.
Niwakudala munthu, ana chikwama chidadzala nawo. An'zanyazisiwa lini, paan'zalewa-lewa naazondi wake pansuwo.
Pamwepo wana wathu kuwubwana wawo, an'zakhala ninga mbewu zakukhuma; wana wathu wachikazi an'zachita ninga ntsigilo zam'magonyo, zidatemelewa kumanga n'zinda;
Koma ine ndili ninga muolivi wakupsipila munyumba ya Mulungu. Nin'themba nantsisi za Mulungu kufika lini nalini.