3 Koma Judha adati kwaapayi wake, “Mwamunayo adatichenjezelatu, adati, ‘Mun'zawona lini nkhope yangu, kunja kwakuti mwabwela namung'ono wanu.’
Paadadya chakudya chaadabwela nacho kuchoka ku Ijipiti, apayi wawo adati, “Yendani pomwe mukagule chakudya ching'ono-ng'ono.”
Koma mukatituma pabodzi namung'ono wathu, tiniyenda kakugulilani chakudya;
koma mukalamba kuti tiyende naye, nayisembo pomwe tiniyenda lini, pakuti mwamunayo adati, ‘Mun'zawona lini nkhope yangu, kunja kwakuti mwabwela namung'ono wanu.’ ”
Pamwepo imwe mudati kwaalanda wanu, ‘Mukaleka kubwela namung'ono wanuyo, mun'zawona lini nkhope yangu pomwe.’