21 Wanthu adati kwa Joshuwa, “Nee! Ise tin'zatumikila Chawuta.”
Mukasiya Chawuta muchikatumikila anango amilungu wachilendo, iye an'zakulinzani ngoto achizakulangani, an'zakumalani, an'zakuchitilani bzakuyipa, pambuyo pakukuchitilani bzabwino.”
Pamwepo Joshuwa adati kwayiwo, “Imwe mwabzichitila umboni mwekha kuti mwasankhula kutumikila Chawuta.” Iwo adati, “Inde, ise takhala mboni.”