Peno bzidayipa m'maso mwanu kutumikila Chawuta, lelo sankhulani wamunfuna kutumikila, panango kutumikila amilungu akhapemphelewa namakholo yanu mudziko lakung'ambu kwakamadzi ka Ufuratesi, panango amilungu waa Amori wamudziko lino lamukukhala. Koma ine nabanja langu tin'zatumikila Chawuta.”