Biblia Todo Logo
Bìoball air-loidhne

- Sanasan -




Joshuwa 20:3 - Bhukhu la Kuyamba

3 kuti munthu akapha mwanzake mwakusaya kudziwa, munthuyo athawe apotele kumweko kuti alombolewe kwaabale wamunthu waadapha kuchitila kuti angabwezelembo kutayika kwagazi lam'bale wawo.

Faic an caibideil Dèan lethbhreac




Joshuwa 20:3
8 Iomraidhean Croise  

“Wuza wanthu wa Izraeli kuti asankhule maguta yakupotela, kuteyeza kuwuziwa kudachitiwa Mozisi,


Iye angathawile kuguta linango pamaguta yamweyo, achikayima pansuwo ukulu waguta, achikalongosola nkhani yake m'makutu mwaakulu-akulu waguta limwelo iwo ankamutakula achiyenda naye muguta, achimpasa mbuto, iye achikhala nawo pabodzi.


Lean sinn:

Sanasan


Sanasan