Biblia Todo Logo
Bìoball air-loidhne

- Sanasan -




Joshuwa 2:16 - Bhukhu la Kuyamba

16 Iye adati kwayiwo, “Yendani kumapili, kuchitila kuti wakukuteyelani aleke kukugumanani. Mukabisale kwantsiku zitatu, kufikila wakukuteyelaniwo abwelela, muchizayenda ulendo wanu.”

Faic an caibideil Dèan lethbhreac




Joshuwa 2:16
6 Iomraidhean Croise  

Nimpotela mwa Chawuta, ko thangwe lanyi unti kwayine, mbululuka bzin'chita mbalami uyende kumapili,


Pamwepo Rahabhi adaabulusa napazhanela nathambo, pakuti nyumba yake ikhali nkati mwampanda waguta.


Akadidiya wale, adayenda kabisala m'mapili kwaadakakhala ntsiku zitatu, kufikila wakuwateyela abwelela. Amuna akhaateyela adaapsaga munjila zentse koma alibe kuwawona.


Lean sinn:

Sanasan


Sanasan