Biblia Todo Logo
Bìoball air-loidhne

- Sanasan -




Joshuwa 1:3 - Bhukhu la Kuyamba

3 Mbuto yentse yamun'zaponda nanzayo zanu ndakupasani kuteyeza kutsimikiza kwandidachita kwamulanda wangu Mozisi.

Faic an caibideil Dèan lethbhreac




Joshuwa 1:3
4 Iomraidhean Croise  

Kuyambila kuchipululu kufika ku Lebhanoni, mpaka kukamadzi kakulu ka Ufuratesi, nadziko lentse laa Hiti kufika kunyanja ikulu, mpaka kun'nyulila dzuwa, lin'zakhala dziko lanu.


Mozisi ntsiku imweyo adalumbila adati, ‘Chadidi dziko lawaponda naminyendo yako lin'zakhala nthaka yako nakum'badwe wako kufika lini nalini. Pakuti iwe wawonesa chikhulupililo kwa Chawuta Mulungu wangu mwakukwana.’


Lean sinn:

Sanasan


Sanasan